Trending News:
  • Fresh calls for MEC chair to resign
  • Chaponda slams minister over “insensitive” response to passport crisis
  • Malawi reaffirms commitment to foundational learning
  • Nthenda ya Sickle Cell ikuchulukitsa imfa za ana
  • Malawi launches first-ever GBV in emergencies module
June 23, 2025
Yoneco FM
  • Breaking
  • News
    • National
    • International
    • Entertainment & Arts
    • Sports
    • Feature
    • Business
    • Health
    • Chichewa
  • Podcast
    • TIcheze
  • About us
  • Programmes
  • Our Team
  • Contact us
Search for:
  • Home
  • Chichewa
  • Page 2

Boma ladzipereka pofuna kuthetsa njala

October 30, 2024November 1, 2024 Augustine MuwotchaChichewa / NationalNo Comment on Boma ladzipereka pofuna kuthetsa njala

Nduna yowona za malimidwe a Sam Kawale yati boma ladzipereka pofuna kuthetsa njala mdziko muno pogwiritsa ntchito ulimi wothilira. Iwo…

Read More

UDF sinalowe mu mgwirizano ndi chipani chilichonse

October 28, 2024October 29, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on UDF sinalowe mu mgwirizano ndi chipani chilichonse

Mtsogoleri wa chipani cha United Democratic Front (UDF), Atupele Muluzi, watsimikizira akuluakulu a chipanichi kuti palibe chipani chilichonse chomwe akukambirana…

Read More

Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze za ngozi ya ndege

October 27, 2024October 29, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze za ngozi ya ndege

Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera wakhazikitsa komiti yapadera yoti ifufuze zokhudza ngozi ya ndege yomwe inapha wachiwiri kwa…

Read More

Bungwe la MEC lati zipani zisade nkhawa

October 21, 2024October 25, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Bungwe la MEC lati zipani zisade nkhawa

Bungwe la Malawi Electoral Commission (MEC) latsutsa nkhawa za zipani zotsutsa m’dziko muno kuti bungweri liribe kuthekera koyendetsa chisankho cha…

Read More

Boma ladandaula ndi kuchepa kwa chidwi cha olemba ntchito

October 9, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Boma ladandaula ndi kuchepa kwa chidwi cha olemba ntchito

Unduna wa za umoyo wadandawula kaamba kakuchepa kwa chidwi chomwe anthu olemba anzawo ntchito akumayika pofuna kuti anthu awo adzikhala…

Read More

Wachiwiri kwa mkulu wa apolisi Casper Chalera wamwalira

October 9, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Wachiwiri kwa mkulu wa apolisi Casper Chalera wamwalira

Wachiwiri kwa mkulu wa apolisi m’dziko muno Casper Chalera wamwalira. M’neneri wa nthambiyi m’dziko muno, a Peter Kalaya, atsimikizira YFM…

Read More

Anthu 7 amwalira pa ngozi ku Blantyre

October 8, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Anthu 7 amwalira pa ngozi ku Blantyre

Amayi asanu ndi awiri amwalira pa ngozi ya galimoto lolemba mu msewu wa Chileka m’boma la Blantyre. M’neneri wa polisi…

Read More

Dr Usi apita ku Morocco

October 7, 2024October 7, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Dr Usi apita ku Morocco

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, wanyamuka m’dziko muno lero ulendo wa ku Morocco komwe akakhale nawo…

Read More

MCP sibwera ku msonkhano waukulu, yatero UDF

September 28, 2024September 30, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on MCP sibwera ku msonkhano waukulu, yatero UDF

Chipani cha United Democratic (UDF) chatsimikiza kuti chasintha ganizo lake loyitana chipani cholamula cha Malawi Congress (MCP) kuti chidzakhale nawo…

Read More

Wotayira mwana mchimbudzi agamulidwa miyezi 6

September 21, 2024September 26, 2024 Augustine MuwotchaChichewaNo Comment on Wotayira mwana mchimbudzi agamulidwa miyezi 6

Wolemba Lauryn M’banga Bwalo la milandu m’boma la Chikwawa lagamula kuti Maria Akimu wa zaka 20 akakhale kundende kwa miyezi…

Read More

Abambo atatu awamanga kamba kokupha m’bale wawo

September 5, 2024September 5, 2024 Augustine MuwotchaChichewaNo Comment on Abambo atatu awamanga kamba kokupha m’bale wawo

Abambo atatu awamanga m’boma la Dowa powaganizira kuti apha mchimwene wawo Howard Yolamu pomubaya ndinso kumukhapa potsatira mkangano wokhudza malo…

Read More

Apolisi anjata bambo pomuganizira mulandu wogwilira

September 5, 2024September 5, 2024 Smart SochelaChichewaNo Comment on Apolisi anjata bambo pomuganizira mulandu wogwilira

Bambo wa zaka 25, Clever Makina, ali m’manja mwa apolisi ku Blantyre pomuganizira kuti anagonana ndi msungwana wa zaka 16…

Read More

Posts navigation

Previous 1 2 3 Next

STREAM LIVE ONLINE

report issues on gbv:call 5600!

report issues on gbv:call 5600!

Listen to YONECO FM

YONECO FM APP

The Equivalency Determination

trocaire

ISPCAN

Search

Search for:

National Child Helpline call 116

National Child Helpline call 116

subscribe for our breaking news

Loading

Follow Us!

Follow Us on FacebookFollow Us on TwitterFollow Us on MySpaceFollow Us on Blogger

Download the Helpline App

LikeBox

Copyright © All rights reserved.